Home Local News KUMUDZIWA_MARY_MHONE

KUMUDZIWA_MARY_MHONE

by Kuwala Gospel Music
408 views

Mary Mhone anabadwa mu chaka cha 1988 ndipo m’banja mwawo anabadwa ana asanu ndipo iye ndi wachinayi kubadwa ndipo amakhala ku Pretoria dera lotchedwa Haertbeatsport Dam Schoemans Vill m’dziko la South Africa,kumudzi kwawo ndi ku Nkhatabay Chisala koma pano anakhazikika ku Mzuzu.

Mary anayamba kuyimba mu chaka cha 2020 koma chimbale choyamba anatulutsa mu 2022 chotchedwa Alipo Yesu ndipo pakadali pano ali mkati mojambula chimbale chake chachiwiri.

Leave a Comment

kuwalagospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel music. For inquiries contact these numbers 0888 069 117/0983 592 032 or info@kuwalagospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media